22 Ndipo mneneri uja anayandikira kwa mfumu ya Israyeli, nati kwa iye, Kadzilimbitseni, mudziwe mucenjere ndi cimene mucicita; popeza caka cikudzaci mfumu ya Aramu idzabweranso kulimbana nanu.
Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 20
Onani 1 Mafumu 20:22 nkhani