1 Mafumu 20:27 BL92

27 Ndipo Aisrayeli anamemezananso, anali naye kamba, nakakomana nao; ndipo Aisrayeli anamanga misasa yao pandunji pao, ngati timagulu tiwiri ta ana a mbuzi; koma Aaramu anadzaza dziko.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 20

Onani 1 Mafumu 20:27 nkhani