7 Ndipo kunacitika, pamene Hiramu anamva mau ace a Solomo, anakondwera kwakukuru, nati, Alemekezeke Yehova lero amene wampatsa Davide mwana wanzeru akhale mfumu ya anthu aunyinji amenewa.
Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 5
Onani 1 Mafumu 5:7 nkhani