30 Ndipo mverani pembedzero la kapolo wanu ndi la anthu anu Aisrayeli, pamene adzapemphera molunjika kumalo kuno; ndipo mverani Inu m'Mwamba mokhala Inumo; ndipo pamene mukumva, khululukirani.
Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 8
Onani 1 Mafumu 8:30 nkhani