32 mverani Inu pamenepo m'mwambamo, ndipo citani, weruzani akapolo anu, kumtsutsa woipayo, ndi kumbwezera cimo lace, ndi kulungamitsa wolungamayo kumbwezera monga cilungamo cace.
Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 8
Onani 1 Mafumu 8:32 nkhani