1 Mafumu 8:33 BL92

33 Ndipo anthu anu Aisrayeli akawakantha adani ao cifukwa ca kucimwira Inu, ndipo akabweranso kwa Inu, lodi kubvomereza dzina lanu, ndi kupemphera, ndi kupembedza Inu m'nyumba muno;

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 8

Onani 1 Mafumu 8:33 nkhani