1 Mafumu 8:59 BL92

59 Ndipo mau anga amenewa ndapembedzera nao pamaso pa Yehova akhale pafupi ndi Yehova Mulungu wathu usana ndi usiku, kuti alimbitse mlandu wa kapolo wace, ndi mlandu wa anthu ace Aisrayeli, mlandu wa tsiku pa tsiku lace;

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 8

Onani 1 Mafumu 8:59 nkhani