Deuteronomo 24:19 BL92

19 Mutasenga dzinthuzanu m'munda mwanu, ndipo mwaiwala mtolo m'mundamo, musabwererako kuutenga; ukhale wa mlendo, wa mwana wamasiye, ndi wa mkazi wamasiye; kuti Yehova Mulungu wanu akudalitseni m'nchito zonse za manja anu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 24

Onani Deuteronomo 24:19 nkhani