Deuteronomo 26:15 BL92

15 Penyani muli mokhalamo mwanu mopatulika, m'mwamba, ndipo dalitseni anthu anu Israyeli, ndi nthaka imene munatipatsa, monga munalumbirira makolo athu, dziko moyenda mkaka ndi uci ngati madzi.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 26

Onani Deuteronomo 26:15 nkhani