Deuteronomo 5:9 BL92

9 usazipembedzere izo, usazitumikire izo; cifukwa Ine Yehova Mulungu wako ndine Mulungu wansanje, wakulanga ana cifukwa ca atate wao, kufikira mbadwo wacitatu ndi wacinai wa iwo amene akudana ndi Ine;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 5

Onani Deuteronomo 5:9 nkhani