Levitiko 10:4 BL92

4 Ndipo Mose anaitana Misayeli ndi Elizafana, ana a Uziyeli, mbale wa atate wa Aroni, nanena nao, Senderani pafupi, nyamulani abale anu muwacotse pakhomo pa malo opatulika kumka nao kunja kwa cigono.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 10

Onani Levitiko 10:4 nkhani