Levitiko 13:31 BL92

31 Ndipo wansembe akaona nthenda yamfundu, ndipo taonani, ioneka yosakumba kubzola khungu, ndipo palibe tsitsi lakuda pamenepo, wansembe ambindikiritse iye ali ndi mfundu masiku asanu ndi awiri;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 13

Onani Levitiko 13:31 nkhani