Levitiko 13:49 BL92

49 ngati nthenda iri yobiriwira, kapena yofiira pacobvala, kapena pacikopa, kapena pamuyaro, kapena pamtsendero, kapena pa cinthu ciri conse copangika ndi cikopa, ndiyo nthenda yakhate; aziionetsa kwa wansembe;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 13

Onani Levitiko 13:49 nkhani