Levitiko 13:5 BL92

5 ndipo wansembe amuonenso tsiku lacisanu ndi ciwiri; ndipo taonani, monga momwe apenyera iye, nthenda yaima, nthenda siinapitirira pakhungu, pamenepo wansembe ambindikiritsenso masiku asanu ndi awiri ena;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 13

Onani Levitiko 13:5 nkhani