Levitiko 17:5 BL92

5 kotero kuti ana a Israyeli azidza nazo nsembe zao, zimene aziphera kuthengo koyera, kuti adze nazo kwa Yehova, ku khomo la cihema cokomanako, kwa wansembe, ndi kuziphera nsembe zoyamika za Yehova.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 17

Onani Levitiko 17:5 nkhani