Levitiko 19:22 BL92

22 Ndipo wansembe acite comtetezera ndi nkhosa yamphongo ya nsembe yoparamula pamaso pa Yehova, cifukwa ca kucimwa adacimwaku; ndipo adzakhululukidwa cifukwa ca kucimwa kwace adacimwaku.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 19

Onani Levitiko 19:22 nkhani