Levitiko 19:29 BL92

29 Usamaipsa mwana wako wamkazi ndi kumcititsa cigololo; lingadzale ndi cigololo dzikoli, ndi kudzazidwa nazo zocititsa manyazi.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 19

Onani Levitiko 19:29 nkhani