Levitiko 23:14 BL92

14 Musamadya mkate, kapena tirigu wokazinga, kapena ngala zaziwisi, kufikira tsiku lomweli, kufikira mutadza naco copereka ca Mulungu wanu; ndilo lemba losatha mwa mibadwo yanu m'nyumba zanu zonse.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 23

Onani Levitiko 23:14 nkhani