Levitiko 23:36 BL92

36 Masiku asanu ndi awiri mubwere nayo nsembe yamoto kwa Yehova; tsiku lacisanu ndi citatu mukhale nao msonkhano wopatulika; ndipo mubwere nayo nsembe yamoto kwa Yehova; ndilo lotsirizira; musamagwira nchito ya masiku ena.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 23

Onani Levitiko 23:36 nkhani