16 Ndi iye wakucitira mwano dzina la Yehova, amuphe ndithu; khamu lonse limponye miyala ndithu; mlendo ndi wobadwa m'dziko yemwe akacitira dzina la Yehova mwano, awaphe.
Werengani mutu wathunthu Levitiko 24
Onani Levitiko 24:16 nkhani