Levitiko 25:25 BL92

25 Mbale wako akasaukira cuma, nakagulitsa cace cace, pamenepo mombolo wace, mbale wace weni weni azidza, naombole cimene mbale wace anagulitsaco.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 25

Onani Levitiko 25:25 nkhani