Levitiko 25:30 BL92

30 Ndipo akapanda kuiombola kufikira kutha kwace kwa caka camphumphu, nyumba iri m'mudzi wa m'lingayi idzakhala yace ya iye adaigula yosamcokeranso mwa mibadwo yace; siidzaturuka caka coliza lipenga.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 25

Onani Levitiko 25:30 nkhani