Levitiko 25:50 BL92

50 Ndipo awerengere amene anamgulayo kuyambira caka adadzigulitsa kwa iye kufikira caka coliza lipenga; ndipo mtengo wace ukhale monga mwa kuwerenga kwa zaka; amuyesere monga masiku a munthu wolipidwa.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 25

Onani Levitiko 25:50 nkhani