Levitiko 26:36 BL92

36 Kunena za iwo akutsalira, ndidzalonga kukomoka kumtima kwao m'maiko a adani ao; ndi liu la tsamba lotengeka ndi mphepo lidzawapitikitsa; ndipo adzathawa monga amathawa lupanga; ndipo adzagwa wopanda wakuwalondola.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 26

Onani Levitiko 26:36 nkhani