Levitiko 26:5 BL92

5 Ndipo nyengo yopuntha tirigu idzafikira nyengo yochera mphesa, ndi nyengo yochera mphesa idzafikira nyengo zobzala; ndipo mudzakhuta naco cakudya canu, ndi kukhala m'dziko mwanu okhazikika.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 26

Onani Levitiko 26:5 nkhani