Levitiko 6:15 BL92

15 Ndipo atengeko wodzala manja pa ufa wa copereka ca ufa wosalala, ndi pa mafuta ace, ndi libona lonse liri pa copereka caufa, nazitenthe pa guwa la nsembe, zicite pfungo lokoma, ndizo cikumbutso cace ca kwa Yehova.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 6

Onani Levitiko 6:15 nkhani