Levitiko 6:6 BL92

6 Ndipo adze nayo nsembe yace yoparamula kwa Yehova, ndiyo nkhosa yamphongo yopanda cirema ya m'khola mwace, monga umayesa mtengo wace, ikhale nsembe yoparamula, adze nayo kwa wansembe;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 6

Onani Levitiko 6:6 nkhani