Levitiko 7:21 BL92

21 Ndipo munthu akakhudza cinthu codetsa, codetsa ca munthu, kapena codetsa ca zoweta, kapena ciri conse conyansa codetsa, nakadyako nyama ya nsembe zoyamika za Yehova, munthuyo asadzidwe kwa anthu a mtundu wace.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 7

Onani Levitiko 7:21 nkhani