Levitiko 7:35 BL92

35 Ili ndi gawo la Aroni, ndi gawo la ana ace, locokera ku nsembe zamoto za Yehova, analinena, tsiku limene iye anawasendeza alowe utumiki wa ansembe a Yehova;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 7

Onani Levitiko 7:35 nkhani