Levitiko 8:23 BL92

23 Ndipo anaipha; ndi Mose anatengako mwazi wace naupaka pa ndewerere ya khutu la ku dzanja lamanja la Aroni, ndi pa cala cacikuru ca ku dzanja lamanja lace, ndi pa cala cacikuru ca phazi lace la ku dzanja lamanja.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 8

Onani Levitiko 8:23 nkhani