Levitiko 9:3 BL92

3 Nunene kwa ana a Israyeli, ndi kuti, Dzitengereni tonde akhale nsembe yaucimo; ndi mwana wa ng'ombe, ndi mwana wa nkhosa, a caka cimodzi, opanda cirema, akhale nsembe yopsereza;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 9

Onani Levitiko 9:3 nkhani