Yoswa 1:5 BL92

5 Palibe munthu adzatha kuima pamaso pako masiku onse a moyo wako; monga ndinakhala ndi Mose momwemo ndidzakhala ndi iwe; sindidzakusowa, sindidzakusiya.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 1

Onani Yoswa 1:5 nkhani