Yoswa 10:8 BL92

8 Ndipo Yehova ananena ndi Yoswa, Usawaope, pakuti ndawapereka m'dzanja lako; palibe mmodzi wa iwo adzaima pamaso pako.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 10

Onani Yoswa 10:8 nkhani