Yoswa 11:6 BL92

6 Koma Yehova anati kwa Yoswa, Usaope cifukwa ca iwowa; pakuti mawa, dzuwa lino ndidzawapereka onse ophedwa pamaso pa Israyeli; uziwadula mitsindo akavalo ao, ndi kutentha agareta ao ndi moto.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 11

Onani Yoswa 11:6 nkhani