Yoswa 13:6 BL92

6 nzika zonse za kumapiri kuyambira Lebano, mpaka Misirepotumaimu, Asidoni onse; ndidzawainga pamaso pa ana a Israyeli, koma limeneli uwagawire Aisrayeli, likhale colowa cao, monga ndinakulamulira.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 13

Onani Yoswa 13:6 nkhani