Yoswa 22:24 BL92

24 ndipo ngati ife sitinacita ici cifukwa ca kuopa mlandu, ndi kuti, Masiku akudzawo ana anu akadzanena ndi ana athu, ndi kuti, Muli ciani inu kwa Yehova Mulungu wa Israyeli?

Werengani mutu wathunthu Yoswa 22

Onani Yoswa 22:24 nkhani