Yoswa 22:32 BL92

32 Ndipo Pinehasi mwana wa Eleazare wansembe, ndi akalonga anabwerera kucokera kwa ana a Rubeni, ndi kwa ana a Gadi, m'dziko la Gileadi, kudza ku dziko La Kanani kwa ana a Israyeli, nawabwezera mau.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 22

Onani Yoswa 22:32 nkhani