Yoswa 23:5 BL92

5 Ndipo Yehova Mulungu wanu Iyeyu adzawapitikitsa pamaso panu, ndi kulanda dziko lao kuwacotsa pamaso panu, ndipo mudzalandira dziko lao likhale colowa canu; monga Yehova Mulungu wanu ananena ndi inu.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 23

Onani Yoswa 23:5 nkhani