Levitiko 13:2 BL92

2 Ngati munthu ali naco cotupa, kapena nkhanambo, kapena cikanga pa khungu la thupi lace, ndipo isandulika nthenda yakhate pa khungu la thupi lace, azifika kwa Aroni wansembe, kapena kwa mmodzi wa ana ace ansembe;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 13

Onani Levitiko 13:2 nkhani