Levitiko 13:3 BL92

3 ndipo wansembe aione nthenda pa khungu la thupi; ndipo ngati tsitsi la panthenda lasanduka la mbu, ndi nthenda ikaoneka yapitirira khungu la thupi lace, ndiyo nthenda yakhate; ndipo wansembe amuone, namuche wodetsedwa.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 13

Onani Levitiko 13:3 nkhani