Levitiko 13:25 BL92

25 pamenepo wansembe acione; ndipo taonani, ngati tsitsi la cikanga lasanduka lotuwa, ndipo cioneka cakumba kubzola khungu; pamenepo ndilo khate lobuka m'kupsyamo; ndipo wansembe azimucha wodetsedwa ndi nthenda yakhate.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 13

Onani Levitiko 13:25 nkhani