Levitiko 13:59 BL92

59 Ici ndi cilamulo ca nthenda yakhate iri pa cobvala caubweya kapena cathonje, ngakhale pamuyare, kapena pamtsendero, kapena pa cinthu ciri conse copangika ndi cikopa; kucicha coyera kapena kucicha codetsa.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 13

Onani Levitiko 13:59 nkhani