Levitiko 14:13 BL92

13 Ndipo akaphere mwana wa nkhosa wamwamuna paja amapherapo nsembe yaucimo, ndi nsembe yopsereza, pa malo popatulika; pakuti monga nsembe yaucimo momwemo nsembe yoparamula, nja wansembe; ndiyo yopatulikitsa.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 14

Onani Levitiko 14:13 nkhani