Levitiko 14:14 BL92

14 Ndipo wansembe atengeko mwazi wa nsembe yoparamula, ndipo wansembe aupake pa ndewerere ya khutu la ku dzanja lamanja la iye wakuti ayeretsedwe, ndi pa cala cacikuru ca dzanja lace lamanja, ndi pa cala cacikuru ca phazi lace la ku dzanja lamanja;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 14

Onani Levitiko 14:14 nkhani