Levitiko 14:8 BL92

8 Ndipo iye wakutiayeretsedwe atsuke zobvala zace, namete tsitsi lace lonse, nasambe madzi, nakhale woyera; ndipo atatero alowe kucigono, koma agone pa bwalo la hema wace masiku asanu ndi awiri.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 14

Onani Levitiko 14:8 nkhani