Levitiko 15:25 BL92

25 Ndipo mkazi akakhala ndi kukha mwazi masiku ambiri, osati masiku a kuoloka kwace, kapena akamakha kupitirira nthawi ya kuoloka kwace; masiku onse cirinkukha comdetsa cace, adzakhala wodetsedwa, monga masiku a kuoloka kwace.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 15

Onani Levitiko 15:25 nkhani