Levitiko 17:10 BL92

10 Ndipo munthu ali yense wa mbumba ya Israyeli, kapena mlendo wogonera pakati panu, wakudya mwazi uli wonse; nkhope yanga idzatsutsana naye munthu wakudya mwaziyo, ndi kumsadza kumcotsa kwa anthu a mtundu wace.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 17

Onani Levitiko 17:10 nkhani