Levitiko 20:6 BL92

6 Ndipo munthu wakutembenukira kwa obwebweta ndi anyanga kuwatsata ndi cigololo, nkhope yanga idzatsutsana naye munthuyo, ndipo ndidzamsadza kumcotsa pakati pa anthu a mtundu wace.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 20

Onani Levitiko 20:6 nkhani