Levitiko 20:5 BL92

5 pamenepo nkhope yanga idzatsutsana naye munthuyo, ndi banja lace, ndi kumsadza iye, ndi onse akumtsata ndi cigololo kukacita cigololo kwa Moleke, kuwacotsa pakati pa anthu a mtundu wao.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 20

Onani Levitiko 20:5 nkhani