1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Nena ndi ansembe, ana a Aroniwo, nuti nao, Asadzidetse mmodzi wa inu cifukwa ca wakufa mwa anthu a mtundu wace;
Werengani mutu wathunthu Levitiko 21
Onani Levitiko 21:1 nkhani